Aaaaa achakwera zimene ayankhula , ndimomwe likuyendera zikoli sizikugwirizana nkutalitali, from south Africa
@hassanrasheed1379Ай бұрын
Koma President chakwera aaa awa nde fundo alibe Bwelera zokha zokha.
@sungananigondwe2807Ай бұрын
Koma mbuzi iyi yimapepelesa anthu 😂😂
@enockbanda4530Ай бұрын
Malamulo adziko LA Malawi 🇲🇼 amaphinja osawuka olemera kundende sakhara koma okupa nkhuku ndi Ena osaukawo. My Malawi my pain but is one day we gonna see
@user-jb5yb9wq3yАй бұрын
Apolice 6000 enao ndi anyamata a youth osati Apolice, tikumana pa ground
@jameskachulu8141Ай бұрын
Koma achitetezo chilipo dzikomo?
@JonesChingaya-yf4ggАй бұрын
Kodi Chakwera uli ndi umunthu koma, milomo ya mtundu wanji yosatopa ndi bodza, sikuchulukatu kwa a police komwe kumabweretsa chilungamo m'dziko koma one's commitment.
@thomasbodo4099Ай бұрын
He is the worst president Malawi has ever had you must go it's a matter of time
@JackMvura-ik2tdАй бұрын
Sanje sipindula wakutokosa umaphabawo zibale athu alubino muyambilaso akachoka not in his time forget
@yassinnandera5634Ай бұрын
😅
@Henry-vw2czАй бұрын
Aaaaaàaaaa mbudzi iyi
@ChimwemweBottomani-hc5juАй бұрын
Sugar akupezeka ku zimbabwe wa mlw akutuluka bwanji sugar apolice alipo ....lamulo lake liti
Komotso amene akuombela manja nawo alibe dzero akukupasani chani chakwera kuba ndichimene akuziwa
@user-bs5yp3un1mАй бұрын
Akurakhura ngat aribetu mabwara
@HarrisonMwanga-xy4scАй бұрын
Mpaka utagonati. aaaaa uyu wakwa,chiozadi ndithu.
@leveltrapper4322Ай бұрын
Paja amangobwebweta2 😂😂😂😂 kd Malawi akulamulira ndi UTI kd
@user-le9su3mt7rАй бұрын
Zoona mbuzi yamuthu kkk
@user-hq6dq7zr1eАй бұрын
Aaaaa apa nde kayano 😅
@TadalaJuwaoАй бұрын
Tiziopa uniform kuti azitichitira nkhadza?
@thomasbodo4099Ай бұрын
He is a president by Speech not by action
@carlossadimba595Ай бұрын
Lamulo likhale la mphamvu kuposa ndale .....koma andale ndi omwe mumaononga police I was watching Mp from mangochi who instructed office of police to transfer police officer that was abuse of power by the member of parliament ....
Ena uniform ikuwakhwepa nde aopedwa bwanji 😂😂😂😂 zopepela galu iwe.. Uphele basi.
@sandimizeka3199Ай бұрын
Amenei nchisilu
@rashidadan2533Ай бұрын
Ma comments mukalandila, muzimuonesa chakwelayo aziwelenga ekha , In Africa , this kind of president we call him ldiot , Bcose all members of MCP who're under case of corruption are free .
@Jermah51kenniasАй бұрын
😂😂😂😂
@henryhenry5369Ай бұрын
Ku Mpoto ndi MCP who ever say he's DPP go to hell and we make sure MCP win every vote . I hate APM and the DPP plus Namalomba. You 2 guys don't come to Mpoto ndipo muzawona nyekwe
@chiswamemo2186Ай бұрын
Or wapolice yo yekha akuchita kuti mbwelera zake iziii 😂🙌
@Jermah51kenniasАй бұрын
A youth amenewo ukufuna azitichitira nkhanza tikamamuzuzula
@user-is5dl7np9gАй бұрын
Mumanga Liti malawi watsopano poti muli pa ulendo pano lamulo liribe mphavu chili ndi mphavu ndi chipani kagwere uko chakwera mbuzi
@user-fs1qo2yd9yАй бұрын
Kod amamulembela ndindani uyu kkkk
@user-uv1vu6ub5o28 күн бұрын
Kuyakhula ndikosavuta eish
@HanishaissahKagansaАй бұрын
Awanso ndiye ayi
@kelvindicksonАй бұрын
Kodi kumakhalanso Amayi achipani koma amawapasa nsalu za Malawi police eti
@IsaacKulongwe-ol5mxАй бұрын
U can point a finger at someone forgetting that 4 fingers are pointing at u
@user-cb2cv9fz7mАй бұрын
Apolice ake mbava Zo zaziii, wakuba iwe nthawi yako yatha ndipo ulibenso mfundo apa nde bolanso bon kalindo Ali ndi mfundo, mbuzi ya munthu chakwera
@WisikiBlack-gj4guАй бұрын
Kodi iweyo ndeukukwanilitsa malamulowo, bwanji mumangolakhula koma osachita
@FOSTERLUPIYA-zc1xvАй бұрын
Kunyoza mtsogoleri wa dziko ndi tsoka pa maso pa Mulungu.Ndipo sizabwino kutero .
@user-mq5vs4hn6oАй бұрын
Machende ako
@user-qv4ko6ps4jАй бұрын
Ntchito ya umbava ndi uchigawenga ndiyo u police choncho apo waonjezela zigawenga za MCP mu chisankho cha 2025,,,,,, Wa satanic we ungalephere kulimbadi mtima, siuja umkati mkalephela kuwina ndikhetsa mwazi! Lero ukungochititsa ngozi ponseponse ,kod ngongole udatenga cash mu 2020 ija kut udzabweze magazi ija kod siudamalizebe?
@jamesgama5489Ай бұрын
Iziwopedwa unform yong'ambika akumavala yoperepesekayi makamaka ku PMF 😢😢😢
@TadalaJuwaoАй бұрын
Achinyamata amene akumavala t shirt ya MCP akumalandira ma 7000 msonkhano ukatha
@user-zk7jw9up6mАй бұрын
Mulibe mfundo zomveka mungobweleza bweleza
@SolomonNjolomoleАй бұрын
Km chimene akuyankhula iyeyu akuchidziwa ?uyuyu ndi bulutu la munthu
@user-mk7fh5ml8sАй бұрын
Apapo ndavomeleza kuti ku Malawi tilibe President ndizoonadi.
@henryhenry5369Ай бұрын
Chakwera is the best DPP wait for Jesus to come. And you have an aggry APM . And amatipatsa manyazi ku UN