Ndili ndi pempho Kwa ayini channel itchi zingatheke your photo isamakhalepo muziseye video isewele full screen please chifukwa zomaonela half ayi ndithu sizabwino we link your channel but when you end up put your face in the TV it's good please my brother and you always poster the good things and we are happy for that's If it's need to show your face I mean like your on video I understand but something like this leave the TV play it self we thought your face my apology
@user-nx9zx6fv4i29 күн бұрын
Channel Ichi ndichabwino Koma kachithuzi Kanu pakonapo mzichotsa mwachitsanzo muluzi TV samayika nkhope ndipempho
@OwenWalter-nz7uoАй бұрын
Bro tamachosani nkhope yanuyo sizikumaoneka bwino plz siyani vidio ichite play payokha plz plz
@@Betty-fe9ql 😃😃😃😃Nanga akufuna azitinamiza ifeyo kutiona Ngati oputsa??? Akhaula ifee ozawina tikuudziwa Kale president wathu ndi Peter Munthalika basi, president osasankha odziwa mavuto amphawife
@patriciacraiton-sf5vu29 күн бұрын
@@user-uc1pd1tc2x😂😂😂😂😂
@EphronJames24 күн бұрын
,
@ibrahimalfred6539Ай бұрын
MCP just forget Malawian the won't vote you trust me
Mukufuna ku gulira azitsogoleri magalimoto tilindi ana mmamizi amene akulephera kupitilinza maphunziro awo chifukwa chosowa nthandizo ra ndalama and tili ndi amphawi oti Oro fertilizer wa pukoni sakwanisa kugura otsathandiza anthu amenewo bwanji mulibe mfundo Achaima Banda
@user-tn5eq9fp2z29 күн бұрын
Akuti ma fortune 😂😂😂 ndalama za boma zipite basi
@NumbDee28 күн бұрын
APM My vote
@edenngoma821427 күн бұрын
Chayima Banda is very intelligent man and you deserve to be Secretary General
Kodi ndiwe wa MCP iweyo.Ndikunena mwini wa channel iwe.Yes or No can be a better answer
@innocentmanyera186128 күн бұрын
ukadziwa ufuna utani
@FosterChakanga27 күн бұрын
@@innocentmanyera1861 ndikufunsa mwiniwake
@FefieTenisha-du7ge24 күн бұрын
Empty manifesto that won't take ordinary Malawians anywhere.. The hopeful SG is just focusing on party members especially those bearing seats of power.. Flashing money,cars etc to office bearers won't take Malawians anywhere... I wonder what Western education does to our minds!!!
@JonesChingaya-yf4ggАй бұрын
Kodi iwe Chaima Banda, magalimoto ukufuna kugulira anthu a chipaniwo ndalama zake uzizitenga kut nanga ziziwapindulira chani amalawi omwe akuvutika ndi njala mdziko muno, iweyo Chaima Banda unamva kut, kut njala amaipangira campaign????
@innocentmanyera186128 күн бұрын
cedetish colours fwetseki
@user-iu7gr2hj1jАй бұрын
Vuto la MCP imakonda chipani osati a Malawi
@paulpaseli6310Ай бұрын
Naye akuyakhula Ngati chakwela 😂😂
@AbdulmajeedJbanda-oz3jvАй бұрын
😂😂😂 musaiwaletu paja ndi chief advisor a chakwela
@georgengwira315219 күн бұрын
Nyawu izi 😂
@user-lk8kj9zv6xАй бұрын
Tinamva kale zonsezi DC anafotokoza kale kut kwabwela magalimoto ndalama zathu zomwe mukutibelazi palibe chachilendo tinamva zonse ndi Bon kalindooooooo Dangerous child
Zinangowona kuchitika kuika pampando zidzetezi or ine school mulibe ndikutha kuonanso mchere mulibe umu tinabetsa ndithu my word is park & go 2025 na chikho ichi chitipitikire ndilo khumbo langa 😏😩😫😵
@JafaliAjusa-zg2xiАй бұрын
Bwerlesani ma galimoto anthu azifa ndi njala anthu oipa Inu
@samsonhavenoyayshonga2609Ай бұрын
Kkkkkkk Koma Ku MCP akusowa ndi chonena kukhala ngati akuzitsusa okha,akudziwa kuti ndiolephera
MCP ichoke zoona koma ku voterani DPP nde sibdingachite mistake yotero😂😂😂
@robertchitsulo8006Ай бұрын
Akulu awa aaaa ndioyakhula kwambiri mkaka uja ndiwabwino zingomvuta aribe Matama . Mwa awa mulibe usogoleri sure koma kuyakhulalitsa
@emmanuelchavula7144Ай бұрын
Fundo zosamveka zoti sizingatukule dziko personal interest 😢 aaaaaa SKC my vote these people must respect that guy otherwise fundo ambiri mwaiwo they cannot convince Malawians to vote for mcp no way
@thomasbodo4099Ай бұрын
Bodza la mbale wawo ndende ndilimene akunenaapali
@YohanePatrick-lc2lqАй бұрын
Kodi mcp ikufuna chani kumalawi poti alephela kale ndiye akupangatso ndale akufuna kumalidzilatu dzikolo ifetu sitikuwafuna sugar paka 4000 y iwe chakwela ulekeletu kupanga kapeni galu
@raytavares2256Ай бұрын
What about buying aeroplanes for Malawi than just buying cars while people are struggling with money and food including medicines in all government hospitals.
@chipiliromalola638029 күн бұрын
APM MY VOTE 💙
@user-lj3jb6hf9fАй бұрын
Kkkkk koma shaaa
@mcdonaldchikoti9422Ай бұрын
I am afraid that this manifesto is too sweet, it doesn't have sound sources of such income to support all the activities. In such way, depending on grants and well wishes is not sustainable for viability of such activities and growth of the MCP😢😢
@misheckmkandawire3340Ай бұрын
Chaima Banda our president 2030
@LuteSynosАй бұрын
😢😢
@owenmoses9434Ай бұрын
Kkkk muja achitira mwana ukampeza akusakula ndiwo mumphika😮😮😮 manjenje with asingle question from Brian Banda😂😂 mpaka kusintha nkhani kuyamba zakuyela ku mtolangani😅
@williamdaka7926 күн бұрын
Palibe fundo yeniyeni apo ndalama zichoka kuti? Ndiadyera amenewo kugula ma galimoto ndikuthandidza a malawi?
@user-oh5vs1gl4nАй бұрын
awa akupita chaka cha mawachi Adadi ndikatundu awina ndithu
@user-kr1kg5hy9lАй бұрын
Ana awa sangamake.
@mishecksipolo7153Ай бұрын
😢 zaziiiii!, I was thinking kuti muli ndima better policies for the Nation.😮old tired brain full of nonsense.
@TroubleKatsala-jp2liАй бұрын
Kodi mukuwakalipila anthuwao? 😅😅
@user-tn2qg1vs9jАй бұрын
Iwe WA MCP mmalo mokamba zachinga muno mmalawi chaka chino chavuta muli busy ndi magalimoto ndiwe galu kwabas
@MaryTchapo-py4hh29 күн бұрын
Chake ochakwera akulephera kuendetsa dziko cz ma alagizi ake nao ndi olepheranso
@user-xm4pb5sq5v26 күн бұрын
Kodi ndale za maiko akwa nzathu zimakhalanso chonchi???uli ndi kutukula dziko kapena chipani?
@malickjeofly7843Ай бұрын
Kodi anthu amene anangobadwa ndi bodza bas😊
@BostonGwazani-hl3bg27 күн бұрын
Ine ndine area chairman koma sindingakhale ndifundo zofoka ngati izi,uyu sangakhale SG.
@user-dn3gp6yi4y12 күн бұрын
Za pa usilu bs malo mokamba mavuto omwe akukumana awanthu ku mamidzi ndalama mukukambazo anthu amudzi sapezeko kalikotse chipani Cha matama ichi😂
@Boi_sheed97Boi_sheed97-cj7og25 күн бұрын
Mfundo zowauza ana .. M'malo molimbikisa ulimi ali busy kamba zansalu ndiye quantem kkkk kkkk malawians need to change mindset
@user-qx3dd7xt9cАй бұрын
Wait the end not malubwa lubwa wa
@jedoforsure284228 күн бұрын
Chakwela mpaka 2030
@thulanimpphiri6873Ай бұрын
Mukuvera bwino abambo awa akuti kunamizana ku chipani cha mcp ndikochuluka kwambiri ndichifukwa amanamiza mutundu wamalawi. Akuti agula magalimoto komaso kupereka ndalama. Ndalama zo akunena misokho yamalawi ndi akuba. Bwanji ngati ali ndindalama bwanji kugula mankhwala kuzupatala or chitukuko koma akuti agulila anthu magalimoto pali zeru pamenepo mukaona amalawi. Munthu wakulo koma zeru alibe.mcp musamupase mupando ameneyo.
@AbdulmajeedJbanda-oz3jvАй бұрын
29:31 Awa achaima ngati ali a chief advisor a president achakwera mmmmm mmh ndipanja penipeni ndekani zikuvuta kumpandoku mulibekanthu umu mbambadi, achakwera nde mumaphunzira ndimayankhulidwe omwe ? Awa ndi cheif advisor nanga kuli apambuyo pa awa alibwanji sidovu lenileni vuto lotenga anthu opanda upangili maphunzilo ndilimeneli ,sungatenge munthu alibe upangili wa u mananger nkuzamuyi mu office popeza ndimbalewanu ayi chichukwa ameneyi nde supplier wa anthu ali pansi pake ndengati iye mmutu mwake mulibekathu ndekuti onse alipansiwa akhala opanda supply mapeto Ake kampani sipanga ndalama nde ndi izi , simungatenge banjalanu lonse kugwila ntchito m'boma including ndi ana Anu omwe , Kodi pakakhala zosayenda bwino angazuzule ndindani kapena angaletse ndindani , eeeee mwatambalalatu pawudindowu Ngati simuzachoka akulu 9:31