May the good Lord protect our president, president for the poor, the only true and trusted freedom fighter remaining on the ground, the Dddddd!!!!! Cccccc!!!!!!
@user-jw5rx9ze8kАй бұрын
Chitsiru si Bon kalindo, koma chitsiru ndi iwe, mulungu akukanthe mfiti iwe.
@BonfaceBanda-nh7cqАй бұрын
Ngt kuli anthu omwe akuseweresa ndarama za boma ndi abungu omwe ali Ku nyumba ya malamulo
@mayesojameskateteАй бұрын
The DC may God protect you 😢😢
@pmbdepot431Ай бұрын
Zautsiru mulunguso chigawenga chimfutichi nyani iwe ndinu mumapha malubino demeti
Boni Kalindo, A mbuye azikhala Mbali yanu nthawi zonse
@RobertLuka-wy9clАй бұрын
Auzen agalu amenewa aphungu akumalawi ndi mbuzi za anthu
@paulmakaula4937Ай бұрын
Mumumvetse Nankhumwa ngati mmadziwa democracy
@languitoneelias9972Ай бұрын
Ndale zimasaukitsa ukazitengela msuzi onse umatha
@JohnConar-kq4hiАй бұрын
Mcp never win
@Uncle_B265Ай бұрын
Chilungamoo chimadwdwaa
@user-vl5on2lj8bАй бұрын
Zaziphasozo andunawo ndiye angolankhula koma ndizopanda sogolo
@hackwellkagolo6614Ай бұрын
Ha ha ha koma MRB mavuto enieni, asokoneza zithu koma akamayankhula ngati finye, kuzipopa kwambiri koma anthu akukwanisa kuhaka system ya Malawi zachisoni kwambiri
@inessmsiyambiri8517Ай бұрын
Eeeee bon kalindo ndi mwana oopsa kwambiri eeeee mabulubuzana kunyumwa ndi dc
@JafaliAkimu-ll1bfАй бұрын
Nankhumwa ndi chitsiru cha munthu muzimuwona nkhopeyo ngati chiswa bumbu
Chitsilu galu kalindo iweyo ukumanamiza athu kuti iweyo ndi President wa athu osauka ukuwapangila chiyani athuwo iweyo koma udziti ndiwe ntolakhani wakhulu ungakhale Presidenti iweyo
@macmsiska2937Ай бұрын
Zopusa a Malawi
@user-lt3xl7cv5nАй бұрын
Mcp bomaaaaaa
@thulanimpphiri6873Ай бұрын
Ine ndikudabwa mumalo moti aphungu aboma azikhala ndiulemo kunyumba iyi koma ndi amene akuyambisa phokoso. Chimene ndimaziwa ine wosusa ndi amene mwina azipanga phokoso. Kusonyeza aphungu a mcp ali ngati mowa wamasesi
@user-og4oe5yp4wАй бұрын
Bon kalindo atuluka Monday pa 08 April inshallah
@ExcitedCornflowers-nw9ocАй бұрын
Olemekezekaaaa?akhangwaraoooo kkkkkk
@user-cd4df3vg4yАй бұрын
Lazalo ndi anthu ake mwatikwana kwambiri anthu okanika
Bone kalindo anarakwanji nangasi anapitisayekha futiyo a police akwathu yikanakhara mbudzi tikana sinthisa ku zidko Lina pamozi ndi chakwera
@salimmkumakumakitombi-yc7pwАй бұрын
kkkkkkk.koma boma ili fertilizer mpaka April nde akathira mbatatesi chani
@henryphiri6100Ай бұрын
Mulibe utsogoleri mwa Nankhumwa
@JamesSpondoАй бұрын
😢
@eliffagondewe8214Ай бұрын
Zovuta kwambiri
@hackwellkagolo6614Ай бұрын
Zachibwana basi, Moti aphungu awawa amene akutisogolera? Ayi ndithu. Vutoso otsogolera ku wa ku parliament sulibwino or pang'ono. Ma bwalo amilandu mbolaso sindikukuziwa kuti ndi mbali iti imene tinganene kuti ulibwino
@issahkagansamussahАй бұрын
Amc ili ndi nankhumwa.
@user-im4tc9qi4jАй бұрын
Koma apolice or kumumanga uyuyu pali phindu?
@BrightMpahaАй бұрын
Koma chonde amalawi Tien aliyense adzuke coz tikuvutika ndiife osat andale,,,inafe timat simudya ndale koma apapa ndikofunika kulifera dziko lathu chifukwa atsogoleri tili nawowa sakuganizila ife ndipo ndikudabwa amipinga simukupangitsa mbindikiro bwanji kuti Mulungu awakathe onsewa bwa? Mwangoti ziiii,,ku HRDC ilikutko ndi ma dem?mwangoti zii,,MDF ilikut mukuona athu anu akuzuzuka muli zii Mesa mumalimbira kuteteza dziko lanu?lero munthu modzi akukupusitsan pokupatsa ndalama,,anthu kumahaka system inu muli momuno muli ziii,,ma lawyer anthu plus tsogoleri wa nyumba ya malamulo Mulungu akukathen anthu oipa koma musangalaliretu ku mwamba kulibe chanu ndipo panopa ndili mkati mopepherera inuyo kuti akuonetsen za Yobu koma osat mukhalenso ndi moyo
@GanMapiraАй бұрын
Kkkk
@mosesmkolimboАй бұрын
za zii
@user-uc1pd1tc2xАй бұрын
😂😂😂😂Thumba la fertilizer kulipira January mpakana April fertilizer asanatengedwe😂😂😂😂😂😂😂 my Malawi 😂😂😂
@user-vr5jn8sz5rАй бұрын
Timakunyadilani
@serakillo8668Ай бұрын
Za njalazo munamvotera kongeresi
@mabvutochimkondenji910Ай бұрын
chikosa boni karind mmalo mit azithandiza anthu chakudya
@patrickmacheso5062Ай бұрын
Nankhumwa ndi mfiti ya munthu.
@EdwinMabvikoАй бұрын
Wamangidwa ndi Kalindo ndiye Nankhunwa wakhala bwanjiso fiti?
@patrickmacheso5062Ай бұрын
@@EdwinMabviko Ndi amene akupangitsa kuti Tonse Alliance izipanga zinthu zosakhala bwino kwa a Malawi,, sadziwa kutsutsa ku Parliament bola akulandila ma allowance ake.
@inessmsiyambiri8517Ай бұрын
Munvere Kaye kuti akuti chani
@patrickmacheso5062Ай бұрын
@@inessmsiyambiri8517 Ndamveratu and he said no comment which means he doesn't know what to say as a leader of Opposition.
@eliffagondewe8214Ай бұрын
A akwiya coz a speaker anena kuti ayambe kulankhula Navicha🔥
@user-qp9bn5ed5nАй бұрын
Koma abare tiyeni tikondane kuti agaruwa achoke
@issahkagansamussahАй бұрын
Pankhani iyi ya akalindoyi ikutuluka chifukwa choti nsali modzi wa tonse allance then chifukwanso choti amadana naye komano mulungu alowelerepo ndithu
@user-yh3dw6qu7zАй бұрын
Mcp akunya naye bon kalindo.nankhumwa ndi nkhumba zedi
@MmikeeMateyo-kj2pnАй бұрын
Chitsilu galu kalindo iweyo ukumanamiza athu kuti iweyo ndi President wa athu osauka ukuwapangila chiyani athuwo iweyo koma udziti ndiwe ntolakhani wakhulu ungakhale Presidenti iweyo