Kkkkkkk I think some thing is wrong with Chakwera,,,he doesn't know what he is doing.Iye ndiye wachipwirikiti heavy
@YohanePatrick-lc2lq26 күн бұрын
Khope iyi siya u president ayi koma nyawu
@FrynessMoyo-to2du27 күн бұрын
Mbuzi nkhumba nyani like u sukutha kuyendesa Boma
@jonathankwangulero445027 күн бұрын
Simply put Chakwera is in Competent. He has destroyed Malawi. Sad to say, APM was better when himself was average. It just shows how doomed Malawi is. CHAKWERA mmmmmmhu - speechless
Mudapeza zitaonongeke bwanji,popeza zinthu zinali bwino nthawi imeneyo,zinthu zinali zotchipa.Iwe galu Chakwera ndi amene waononga zonse zimene zimayenda bwino nthawi ya DPP
@clintonhodda983027 күн бұрын
Ngati kuli munthu waononga zinthu ndi Chakwera
@user-ln3zx6wo4w27 күн бұрын
Iyeso akufunika kuwongoledwaka
@goodvisionmedia202327 күн бұрын
Aaaaa mbuzi yamunthu iwe nde pomwe anasiyila a DPP ndi pano sukuwona kusiyana pano tili Pati iwe ulibe umunthu ineyo ndichewa tinakuvotela iweyo koma palibe ndinabesa vote yanga 4 year osasitha or kuti adpp anawonoga 4 year is far bro
@thulanimpphiri687327 күн бұрын
Mwasimikiza nokha apule kuti nduna zanu ndizaku church kwanu komaso ndi achibale anu aphungu wose akukuonani kuti inu abwana ndinu ogona mwanena nokha apule kuti anthu sakukuopani Mulungu akusekani kumaso ndi speech mwayankhulayo. Bwana ndinu antchito ndi amene munalemna nokha😂😂😂😂😂😂😂
@jeanbotomani908127 күн бұрын
Anagwetsa economy ndi ndani tikuonanitu
@AustinMbike23 күн бұрын
Munthu uyu ndiye president weniweni wa masophenya akukhazikhitsa zinthu zikuluzikulu zokha zokha, zana lomweli amayakhula za Agriculture, Tourism and minining zomwe sizinamvekepo mu mbili ya zaka 35 zathazo, more fire Mr president akufunika anthu omulimbikitsa. Otsutsawa tili nawo mpaka imfa kumasutsa ndi zabwino zomwe.
@francistsutsu481127 күн бұрын
palinso za bola, apm angatipangire chiani cha nzeru atabwereranso ndi mmene alirimo? Amalawi tiyeni timovereze kusitha maganizidwe athu
@macrinenduna102426 күн бұрын
Kuvomereza zichani? Kodi uyu akamatinamiza kuti Malawi/ ulamuliro wake wakomana climate changes, ku S.A, Moz., Zambia bwanji? Kuitenga wogodomala ife? Tayendani muwone mmene maiko ena moyo wukuyendera. Salary ya aphunzitsi apa Nyasaland ikufanana ndi ya mlonda wa muno Mocambique ukasintha meticas to kwacha. Ndiye nkumavomereza zopusazo. Chakwera komanso mlangizi wake kaya amakhala pansi to verify first a speech to be addressed to a nation as such, a shame.
@MustafaLikaomba27 күн бұрын
Koma galu chakwela kumangopitiliza kwanamiza anthu zamanyi bas
@jameskachulu814127 күн бұрын
Ndiye kuti wa uletsi ndi mwini chakwela yemweyo😂😂😂😂😂galu yomweyo
@LUCKYM478727 күн бұрын
Fact
@Slyvia-uu3wc26 күн бұрын
Kodi amatidyetsa thawi yonseyi anali chakwera patumbo pa make ndithu
@yasitafuphiri-nw2he27 күн бұрын
Chakwera is changing malawi government amicably, by 2030 things will be in right channel 😊
@user-ee6be5kl5o27 күн бұрын
Pulezidenti uyu zoonadi alive nzeru poyankhula angochooka aneneyu ndipo alibe manyazi tulani udindo mwalephera basi osamangodya ndalama Zathu Za misonkho ayi palibe chimene ukuchitila anthu a mmmalawi
@HarrisonMwanga-xy4sc27 күн бұрын
President anati,kwa anthu oputsafe,azatsitha, Malawi pa two years lero, history ingochulukilabe.kuba,kwachuluka Burkina Faso yatenga boma,lawo,ife tilikale.lero, Burkina Faso yatsitha kupotsa, malawi.mr president chilungamo chikuwasoeekela,manyazi bwa?mutu mphwiiii munamizile,ogwila ntchito?
@IsmailBrighton-gm4tl27 күн бұрын
Lkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk ayayaaaaaaaaa
@gminsuranceassesors661126 күн бұрын
Munthu woyambirira kuti akaphunzisidwe ku sukulu imeneyi ndi Chakwerayi akathale limodzi ndi Zamba wakeyo. Anthu omwe akubweresa chipwirikiti ku Boma ndi ma bulutu amenewa.
@user-og4oe5yp4w27 күн бұрын
Komatu munthu amene walemba speech imeneyi Ali pandale zomwe chakwera sakudziwa apa chakwera akuzidzudzira yekha kkkkkkkkk walemba speech imeneyi I salute
Ndiwe opusa kwambiri nthawi ya Peter sitimagona ndi njara koma uyu analowa boma kut adzaphe anthu ndi njara nthawi ya Peter chimanga chimapeza paliponse paja mumkati tikupita ku kenani uku ndi kukenani kepana tili ku guputo chakwera ndiwe galu ulibe fundo