Bwanji Amalora mbudzi Chakwera kulowa dziko la America pamene iyeyo ndye mwini wakubayo
@SymonNamalomba-sh3fu26 күн бұрын
Useless wicked Chief Justice
@FrynessMoyo-to2du24 күн бұрын
Asiya mbava zenizeni
@GeoffreyShariff25 күн бұрын
Ulemu kumpando muyetsesa kutifukulira khani
@PetersonMvahekhe18 күн бұрын
Wosamatinamiza abale
@MathewsMANDUTU-lh6oo25 күн бұрын
Kkkkkkkkkkkk Koma uwu ndi umboni kuti boma la chakwera lazadza ndi m'bava,,,, ndye ena mukamakakila kuti chakwera ukuyendetsa dziko bwino uyu ndi amene ali patsogolo Kuba ndalama amalawi.
@SheenahMwalabu-iz3pr26 күн бұрын
Kodi zoti ukamaika nkhani usamaikepo nkhope yakoyo sizimveka kapena mwano? Kunena zoona umabowetsa program yi and kumangolankhula mwachidule mitu yankhaniyo. Aford munaitha kupatuka nsanga, Nanu a Utm pangani zomwezo changu. Mcp sitikuifunanso next year
@clivendecha855426 күн бұрын
if you really wna people to support your channel, you should remove your chinkhope when u playing the upcoming video.... just do intro then leave the news playing without your face on screen but you can always show up and comment after the news.
@rashidadan253326 күн бұрын
Remaining chakwela and, saulos Chilima ,
@ThokiseWiriyam-ws1ec25 күн бұрын
Mbava zokhazokha
@user-gx5ht9gm3z26 күн бұрын
NO PANI NO GAIN NGAT AMELICA IKUFUN KULESA ANTHU INDAKAYABA KULESA ACHAKWEL NDI ACHILIM
@eliffagondewe821426 күн бұрын
Akukondera apa achina mkaka akuyendera ma galimoto odula asattar chilungamo apa chasowa..
@user-xo2hi3vu8k26 күн бұрын
Tachioneni maso chili phenipheni ngt chiziri plz mukubowesa khope yanu isamaoneke
@user-un6qv6sj3h26 күн бұрын
Mbava chakwera ukutumikira iwe ndiapananja lako gonthi foseki
@eliffagondewe821426 күн бұрын
Chilungamo apo chasowa achina mkaka nanga awsiyilanji?? Ma galimoto akuyendera, a a akangotenga onse omwe Ali pa list paja aaaa
@ChimwemweMagombobanda26 күн бұрын
Chitukuko chilichonse angoti ku Lilongwe basi ,,mavoti muzatengeso komko
@MarthaMalopa-kw9xw26 күн бұрын
Koma Malawi Judiciary ndi nyatwa! Kkkkkkk hahahaha
@user-le9su3mt7r26 күн бұрын
Chakwela mbava chilima boma 2025
@user-wd9yd1bg9n26 күн бұрын
Ife tikuona kuchedwa kuzavotera dpp
@user-sb8hi8vc9w25 күн бұрын
Ika Manda mapaz Anu athu achinyengo inu muzaziona tiyen nazo
@user-gx5ht9gm3z26 күн бұрын
NO PAIN NO GAIN WHAT ABOUT CKWEL AD CHILIM CHINYENGO AMELICA BWANJ IKUSIYA CHAKWEL NDI CHILIM
@DylesMtenje26 күн бұрын
Olo tivote mawa mcp paulendo
@AleksaWilliams-qc6cn26 күн бұрын
Asova a tonsewo
@user-rn7wv8ze3v25 күн бұрын
Malawi akuvuti pano chifukwa cha anthu wozenga milandu