Ndili kumbuyo kwa America. America inapereka mpaka mokwanira kuti tifufudzane tokha koma tarephera. mpaka 4 years kuli ziii nde mumati atani
@robertzambia869723 күн бұрын
Malawi amaombela Maja zili zose akulakhula anyamatawasoo apa zozizila
@user-jk8sh7fh2d22 күн бұрын
Eh eh mpaka 4 years akufufuzabe?
@JonesChingaya-yf4gg23 күн бұрын
Penapake anyamata inu analysis imakuvutani mukuzikolakola kwambiri, ma court athu sakugwira ntchito yawo bwino.Muzikumbukira mlandu wa chisankho anaupasa masiku ndipo zinatheka, milandu ya anthu enawa ikukanika pati kuipasa nthawi????
@tshidikepadisa314822 күн бұрын
imavutadu milandu imeneyo ndi yaliti ma court akumachedwesa dala ku gamula cholinga ayizizilise milanduyo ithele malele munayambila muja wa chilima uku weluzidwa bwanji enawo kuli ziiii
@andreabanda783823 күн бұрын
But for how should we wait for the courts in legal perspectives. Are the judges really working in this country specifically on these matters that USA has complained. Indeed our justice system is too slow.
@user-jk8sh7fh2d22 күн бұрын
Ma Americans ndi owopsya aiona kale nkhaniyo ,ife tikhoza kunena kuti afulumila yes. Koma nkutheka mamulumuzana amene apanga Mack -wa awafufuza kale mwa okha moti ma Americans akuziwa chimene akunena ndithu, moti amene apeleka kalatai kuwafusa akhoza kupeleka umboni ndithu.
@user-jk8sh7fh2d22 күн бұрын
Ndie ma guys kumeneko tisaziikile ku mbuyo system yathu ya ka fukufuku pa nkhani ya katangale ndi zina za mbili si zilibwino ku boma-ku moti kungopemba Mulungu azalowerelepo potipasa anthu owoopa Mulungu bsi
@user-jk8sh7fh2d22 күн бұрын
Komadi inu anyamata kumeneko ku fufuza nkhani ena apa akuti mpaka 4 years akufufuza mulandu , kodi amakhala aku fufuza golide chan ai it's to much ku malawi kuno that's why ma Americans angokuuzani ma wise bsi iya
@user-nj5vu8cd5l22 күн бұрын
Yes it is more than necessary. He has More power to tell them the truth about America behavior
@Cee-H-Cee23 күн бұрын
First to watch
@DaimonJulio-ce8mq23 күн бұрын
Congratulations live from Johannesburg
@abdulsalammkwepu332120 күн бұрын
Vuto ndima court athu they are very very slow when comes to passing judgement, even the issue of leader of opposition is still hanging there. Don't blame america
@francismungu774922 күн бұрын
MCP anagula ma court, police mdf . Zonse ndani sakuziwa kumalawi kulibe justice and democracy. Mcp anaphwanya zonse koma simadolo la 40 lizakwana
@MatSecurity-gq3hr22 күн бұрын
Dziko Ndi Anthu Ake❤
@paulmakaula493723 күн бұрын
Anyamata athu a Times timantha tayamba kuwapeza, their paymasters ayika timinga😢😢
@hackwellkagolo661422 күн бұрын
Chakwera he did mistake kuyankhula pagulu la anthu. Amereka sunayime pachulu but they wrote a letter and to respond anayenelaso alembe kalata. Poyankha mkalata anayenela afufuze bwino ngati President chifukwa vuto ndi lakuti mulandu omwewo wina akuyendela kukhoti pamene ena anangochosedwa m'maudindo awo pamenepo pali kukondela. ACB mwayipha zikugwira tchito yawo ngati momwe inayambila ndiye amereka yakhalangati yalowa m'malo mwa ACB and sinanene kuti amangidwe ayi nkhani ndiyoti anthuwo asazapiteso ku America ndiye inu musanyasidwe kapena kukamila ngati ku Americako ndikwanu. Tiyeni tizidya nandolo kuMalawi komkuno basi.
All world 🌎 there are know that Malawi there too much crampions
@RobertLuka-wy9cl23 күн бұрын
Chakwela ndi mbuzi
@samsonmtumbati485522 күн бұрын
For how long that's why governments of America take actions
@user-oe1lg4xo7w22 күн бұрын
Anyamata atatuinu mmmm pamutupanu palibe nzeru mwadziwika kuti ndinu Ayumi a mcp inunso ndi mbava akufufuzene kumeneko
@bisciouspalima862622 күн бұрын
President sadalakwitse tikati bwanji amalankhula chichewa bwanji samalankhula English zangowonetselatu kuti atolankhani enanso ndi mbiri zenizeni . Chakwera amawuza amalawi a president samawuza america . America adalemba kalata choteronso Boma liyankhanso kudzeranso mu kalata office ndi office .
@apostledavismsosa17 күн бұрын
I dont see any mistake in the lstter wrote with American embacy. Chifukwa Malawi imangoyimbanyimbo pa nkhani ya katangale.Aliyense akakhala pa mpando nkhani ndi kubsa basi. Zimakhala zowawa ngat watumiza thandizo kwa munthu yemwe wafuna kuti lika mufikire kenaka ukamve kuti thandizolo wadya ndiyemwe unamutumayo Makawi ikuonjeza a Merica sikulakwa.
@user-ev6bi7jr7g22 күн бұрын
Milungu ya MCP ili m'makhothi ndipo akhothi ndiomwe akuwononga dzikoli zikukhala bwanji milandu nkumatha zaka 4
@MustafaLikaomba23 күн бұрын
Chakwela ndimbuzi kwabas ozungulila mutu kwabas
@Moses5122 күн бұрын
Akafuna kuyanihula chakwela ndawinzose amayangula chidzungu why him he did speak in chitchewa why
@ThokohKalonga-je9rx22 күн бұрын
ACB yake itiso nanu mesa ili limoz ndi achakwerawo kodi komaso sikugwila tchito iliyonse. Nanunso muli limoz ndi MCP kapena
@user-zk7jw9up6m23 күн бұрын
Amawopa kuti America imumvela zoyankhula zake
@chisosera21 күн бұрын
It is shameful to use power or riches to oppress the poor. American embassy should have contacted Malawi government on the issue if they had a concern. Malawi is sovereign country and is very right to remind America of our independence. Speaking in Chichewa is not wrong, it is also the pride of local language, every other country leader in most Europe and rest of the world speak in there language. Well done Malawi. Mindset change!
@HaroonSaidi-jv3ek20 күн бұрын
What about Uladi mussa why u didn't say that?
@user-nj5vu8cd5l22 күн бұрын
Chakwera moto we want such of African leaders who no fear America
@user-zk7jw9up6m23 күн бұрын
Mbava zokhazokha boma la malawi
@paulpaseli631021 күн бұрын
Times pano inadya chi bazi aaa zinasiya kukoma
@user-nj5vu8cd5l22 күн бұрын
He has rights to speak into his mother's language
@georgejere292222 күн бұрын
Akuopa kuti angamve kkkkkkkkkk😅😅😅😅😅😅
@HaroonSaidi-jv3ek20 күн бұрын
KKKKKKK mmmmm lero ?
@henryhenry663222 күн бұрын
Ma cadet
@chisosera21 күн бұрын
Behaviour without respect
@danielmsowoya910719 күн бұрын
Kaya chizungu Kaya Chichewa komabe wachita bwino kunena chilungamo. Asamatitole azunguwa
@user-nj5vu8cd5l22 күн бұрын
Thank a lot Chakwera to shut America,
@charitymhone998322 күн бұрын
Mmmm nanu inu chakwera angapange shout down America who is chakwera, wasiyilanji kuyankhula mchizungu kt America imve, galu ya munthu... Mumangoombera mmanja ndizopanda pale, zaziiii
@user-hd7wq2yc6m22 күн бұрын
America popanga chiganizo chimenechi choletsa anthu 4 a merica inawona kale kuti boma la Malawi pamozi ndi ma court athu alibe chilungamo pa nkhani yimeneyi anthu 4 amenewa akuchitidwa sheiled ndi boma lathu boma la malawi ndilakuba kwambiri this government is worst than any government we had since mart party democracy, so a Merica is not wrong to burn these 4 people not to travel to their countty a Merica is our big partainer interms of development so a Merica is well montering us on how governmet is using their funds inuso awounder Msiska simumayha kumasilira bwino nkhani mumakhotesera daladala kaya boma lanuli linakudyetsani kamba ku kamwa kwanuko, mlandu mpaka 4 years ma court akutani? Kuzengerezera dala, ACB ilikoso kino ku Malawi? a Merica should contnue to burn those who have been left out including himself chakwera pa anthu onse aja anatchulidwa chilima yekha kuimbidwa mlandu? Onse aja amatchulidwa 79 alikuti? This government is worst than any governmet we had since mart party government from 1994 useless government
@AbuOsman-ts6ef22 күн бұрын
Mantha awo
@hakimbaiton22 күн бұрын
2:20
@MikeKachiwala-ln5vp22 күн бұрын
You guys you must know that Malawi is dying slowly because of corruption.
Koma anakayankha nchizungu ndi nchichewa momwe. I remember how Bingu responded to Americans interms of Malawi economy. Chakwera knows himself he's a puppet, he can't even stand and show his anger over America.
@bisciouspalima862622 күн бұрын
Pamene paja amalidziwitsa dziko lamalawi lo mwe iye ndi president . America idatulutsa chikalata nawonso boma awayankha kudzeranso mukalata