ZOMWE AYANKHULA A MUMBA MOSAOPA🔥🔥🙌🙌

  Рет қаралды 53,884

HOT 265

HOT 265

Күн бұрын

Пікірлер: 122
@RichardChirwa-em6qj
@RichardChirwa-em6qj Ай бұрын
Mbuzi ya Msogoleri kugona posaka ndege koma za nyasi tulo nkupirira shame charakwe
@MrsNankhumwa
@MrsNankhumwa Ай бұрын
Osamatchula dzina la Mulungu pachabe, akukuonanitu Mulunguyo komanso akumva,
@LawrentNyasulu
@LawrentNyasulu Ай бұрын
Opule kuchisankho ndye kuchezera koma kosaka ndege osapitako
@chesterphiri7523
@chesterphiri7523 Ай бұрын
Good question indeed
@CatherineDesire
@CatherineDesire Ай бұрын
Eeetu akuti kkkkkkl
@MEGANABIGAILMNTHALI
@MEGANABIGAILMNTHALI Ай бұрын
I like the point brother
@mikebernabechimundi3472
@mikebernabechimundi3472 Ай бұрын
Ndi ma kape ma assassin
@GodsFavourite1
@GodsFavourite1 Ай бұрын
Maka maka mmmmh
@user-vv6rv4it4j
@user-vv6rv4it4j Ай бұрын
Kuchezela kumeneko koma kosaka dege ndiye malile 6 koloko
@user-mf5ce9wj4m
@user-mf5ce9wj4m Ай бұрын
I'm not supporters of MCP but when it comes to Mr Mumba I support him all the way to 2025 all the best for him.❤❤❤
@quoniemagalasi9123
@quoniemagalasi9123 Ай бұрын
I salute to Chithyola for such speech.. he is composed in his speech
@MarthaMbewe-uk5nn
@MarthaMbewe-uk5nn Ай бұрын
KOMA LERO MULUMGU NDIYE AKUTCHULIDWA BWANJI??😂😂😂
@rhonardmalipa4712
@rhonardmalipa4712 28 күн бұрын
Kuzimva, ati I have never lost , sizingatheke , aaaaaaa ,Mulungu amadana ndi perfectionism kaya
@samanthamuller7643
@samanthamuller7643 Ай бұрын
Mr chikangawa munamusiya chilima akumwalira uku unsiku onse
@EmmanuelClementKhumalo
@EmmanuelClementKhumalo Ай бұрын
Mbuzi iwe
@YellowmanMalawi-qe8zh
@YellowmanMalawi-qe8zh Ай бұрын
Chithyola nkhopeyo koma ndalama imamuonesa kukongola munthu
@PeterKhumbilaZimba-ql9ue
@PeterKhumbilaZimba-ql9ue Ай бұрын
All the best Mumba akubwera boh keep on Pushing Sir.
@masalinodovu1705
@masalinodovu1705 Ай бұрын
Bakili muluzi tv is loading.......
@LonnieMdulamizu
@LonnieMdulamizu Ай бұрын
Zovesa chisoni achilima anagona okha muchikangawa inu apule mwagona uko hmmmm mukuyalukatu tionana 2025
@user-hl3st3cc4v
@user-hl3st3cc4v Ай бұрын
Apa ndekuyakhula ngati Angelo anthu iyipa inu mukawinamo munyele moto
@pauljosephmakaula6835
@pauljosephmakaula6835 Ай бұрын
Speech ya abwana inapangila campaign gulu lina and directly DECAMPAIGNED our Engineer Mumba! Bwana Mumba ur ideologies fits into another popular innovational party...PITANI ndithu u running mate ulipo
@OfwaMwambila
@OfwaMwambila Ай бұрын
Happy to see my childhood buddy.vitu u where bon to be a leader.ur leadership skills goes where back
@lupakishomalangaelix6606
@lupakishomalangaelix6606 Ай бұрын
Ulipo nganya?
@user-vf4yo6gt6q
@user-vf4yo6gt6q Ай бұрын
Chithyola is cool calm and collected
@JaxyKumwenda
@JaxyKumwenda Ай бұрын
Mumba anayikonda MCP koma MCP sidamukonde abwere ku UTM ndikomwe ndikomwe kufunika anthu atsogolo labwino
@BatumeyoChikopa
@BatumeyoChikopa Ай бұрын
Lelo mukutchula Mulungu ndi anthu akumudzi ovutika😊😊😮
@WanangwaMfune
@WanangwaMfune Ай бұрын
Zinaziwika kare Kuti mumba akawina nchifukwa amatchingatchinga koma amati chomwe chidzakhala chako nchako basi or mundikhomelere..❤️‍🔥❤️‍🔥❤️‍🔥❤️‍🔥
@SueWahna
@SueWahna Ай бұрын
Osatekeseka MR mumba
@HappyNkhatha
@HappyNkhatha Ай бұрын
VP iyo yilute kumpoto kwithu lero .Mumba is the best future
@RightwellZumbwe
@RightwellZumbwe Ай бұрын
Kkkkkkk koma chithola ndewathyokatu
@Syakinongwa
@Syakinongwa Ай бұрын
I wish I could know more about more of Chithyola. So patient in speech. Full of knowledge. Love you bro.
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Ай бұрын
Mr Chithyola Man of god indeed Madzulo ndi Sabbath osaiwala kukasegulila sabbath
@BunaahAdamh-q2v
@BunaahAdamh-q2v Ай бұрын
😂😂😂😂😂😂 usachule mulungu iwe wabesa ndalama
@AllanWilsonbanda
@AllanWilsonbanda Ай бұрын
Koma akuvetsatu chisoni maonekedwewo
@MakandeMpambalika
@MakandeMpambalika Ай бұрын
Mumba so corregous
@TaniaMphalumo
@TaniaMphalumo Ай бұрын
Chicholayo akugona uku akulila garu iwe
@Biath-m4b
@Biath-m4b Ай бұрын
Mumba well done iwe anthu amakuopa kt ungawine but God is one amamenya nkhondo iwe uli chete
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Ай бұрын
Agwesedwamo umu
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Ай бұрын
😂😂😂😂Chinthyola tsopano kuyankhula mwanzeru komanso modekha 😂😂Mulungu amakumbukiridwa nthawi yamabvuto
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Ай бұрын
I wish all the best to Mr Chithyola to won....
@emmanueljelemani4203
@emmanueljelemani4203 Ай бұрын
Wishing you all the best Mr Mumba🎉
@FrankNyirongo-d6n
@FrankNyirongo-d6n Ай бұрын
Ziphanapopano zokhazokha
@RobertNyaude
@RobertNyaude Ай бұрын
🔥🔥 Mumba
@PatrickMalaw
@PatrickMalaw Ай бұрын
His grace is indeed sufficient
@LindaNkwazi
@LindaNkwazi Ай бұрын
Koma chithyola boza
@GodsFavourite1
@GodsFavourite1 Ай бұрын
Mulungu mukumutchulatchulatu a chithyola
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Ай бұрын
Kkkk
@MercyMithie
@MercyMithie Ай бұрын
Mumuyèse chimwendo BP
@WisikiBlack-gj4gu
@WisikiBlack-gj4gu Ай бұрын
Kkkkkk mumaopa allah inuyo inuyo,, ndekuti mulungu amakutsogolelqni pakuba mu bomamo
@FrankNyirongo-d6n
@FrankNyirongo-d6n Ай бұрын
All the best
@user-io2uw2me9f
@user-io2uw2me9f Ай бұрын
First comment
@MemoryMbepula
@MemoryMbepula Ай бұрын
Mumba is geneous
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
Achithyola 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂Koma ndaseka 😂😂😂😂😂😂😂😂
@user-xz3nz7dy1f
@user-xz3nz7dy1f Ай бұрын
Achimwendo kodi mudaziwa kt Mumbayo chimamuna hahahha mamuna zako pa chulu kulinga utakwerapa
@user-xs3nj1es1r
@user-xs3nj1es1r Ай бұрын
Kkkkk chithyola mutu sukugwila😂😂😂😂
@SydneyNyasuli
@SydneyNyasuli Ай бұрын
Kkkkk anyamata
@Martha-m6e
@Martha-m6e Ай бұрын
More fire Times ❤❤❤
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn Ай бұрын
Akusidza achithyolawo😂😂😂
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx Ай бұрын
Stress ikuwatibula chisankho mchoopsa
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx Ай бұрын
Apa awine Richard chimwendo Banda
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂Koma guys​@@PaulChaleka-lb4vx
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
😂😂😂😂Uyu bp yakwera
@FrancisStima-sc7zs
@FrancisStima-sc7zs Ай бұрын
Mumba more fire, 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@SelinaGamaliyere-q8v
@SelinaGamaliyere-q8v Ай бұрын
Achitchora kuyankhula ngati mgelo mbava yachabe chabe
@FrankAdonis-zl6qc
@FrankAdonis-zl6qc Ай бұрын
Mbava yotheratu
@user-pn6ic9yr1t
@user-pn6ic9yr1t Ай бұрын
All the best mumba
@CharlesPembaMusaiwale
@CharlesPembaMusaiwale Ай бұрын
Mulungu wasankha kale enafe timangokwanilitsa chabe
@amalauantonioantonio4056
@amalauantonioantonio4056 Ай бұрын
Positive❤
@RobertMwafulirwa
@RobertMwafulirwa Ай бұрын
Chithyola ndodekha chonchi? He has spoken very well
@jomochirwa
@jomochirwa Ай бұрын
Chithyola is not suit for sg .mulembi wachipani amafunika kukhala munthu wa ma vuvu monga chimwendo.
@SuzgoMunthali
@SuzgoMunthali Ай бұрын
Mwabesa ndalama inu 😢😢😢😢😢
@TywellShumba
@TywellShumba Ай бұрын
Koma chimwendo ndi mbuzi ndamuonadi 😢😢😢😢😢
@MercyMithie
@MercyMithie Ай бұрын
Chithyola wakumbuka mulungu 😂😂😂😂😂😂😂
@RacsonKundambo
@RacsonKundambo Ай бұрын
Ndalama zomwe amabazo lero zabwelera kwa anuwake amene ali anthu akumudzi omwe amati akawavotelewo
@TywellShumba
@TywellShumba Ай бұрын
Mumazitenga ngat mli ndi maudindo Akuma company koma akukusangan ndi anthu omwewa mkuwatenga ngat agalu anu pano munya
@martinsailesi1731
@martinsailesi1731 Ай бұрын
Wakupha amafanso end of errs
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q Ай бұрын
Anamuletsa Kani amawopa 😂😂😂😂😂
@SuzgoMunthali
@SuzgoMunthali Ай бұрын
Kumbuka mulungu pa mavuto basi 😅😅😅😅😅
@FranciscoJendala
@FranciscoJendala Ай бұрын
koma chitchyola walankhula bwino modzi chepetsa mogwira mtima. akuoneka umunthu ulimo osatikulankhula mwamtudzi , kuzichemerera a yi
@TroubleKatsala-jp2li
@TroubleKatsala-jp2li Ай бұрын
Kumafunsamutaimapatalitu chifukwa enao akumenyani kkkkk
@user-ld8gb9xm7v
@user-ld8gb9xm7v Ай бұрын
Onse a MCP ndiokuda thupi ngati makala
@munashemoyo4190
@munashemoyo4190 Ай бұрын
Koma chithyolayo sakomoka uyo 😅😅😅😅😅
@BennettNjedza
@BennettNjedza Ай бұрын
Mulungu mukumufuna lero😅
@user-hh4wn4vf9e
@user-hh4wn4vf9e Ай бұрын
😂😂😂chitchola sawina😂😂😂
@JasonMailos
@JasonMailos Ай бұрын
Kkkkkkk kupemphezela? Anyamata mukuyakhula
@kennedybanda
@kennedybanda Ай бұрын
Mulungu muzonse kumene.
@stanleymatolabanda5460
@stanleymatolabanda5460 Ай бұрын
A chityola akuchita kumvetsa chisoni 😅😅
@amalauantonioantonio4056
@amalauantonioantonio4056 Ай бұрын
Positive
@robenmatchilinga604
@robenmatchilinga604 Ай бұрын
Kkkk khope za mcp szimasowa 😂😂😂
@CatherineDesire
@CatherineDesire Ай бұрын
Ameneyo chityolayo ma 50 kg pa airport zimapita kuti,wayambaliti kuthandidza,thandidzo amapeleka nthawi ya campaign kodi thandidzo mesa amathandidza pofunikira thandidzo 🤔👀🙄
@LeviChakwira
@LeviChakwira Ай бұрын
Chipani ichi nchoipa kwambiri. Anthu okupha
@daviechapweteka4759
@daviechapweteka4759 Ай бұрын
Okay
@AmosScott-z9x
@AmosScott-z9x Ай бұрын
Amumba paja mumati simunaluzepo eti
@JosephChikabadwa
@JosephChikabadwa Ай бұрын
Mfiti sisambitsa maliro
@user-ln5hw7dn9g
@user-ln5hw7dn9g Ай бұрын
Mumbaaaaa
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q Ай бұрын
😂😂😂😂😂💪💪💪💪💪💪🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@MillieMalakam
@MillieMalakam Ай бұрын
Mcp ndi ndi chipembezo chokuba
@gkay-striker
@gkay-striker Ай бұрын
Anthu opoila inu zianthu zoipa izi
@MarthaMbewe-uk5nn
@MarthaMbewe-uk5nn Ай бұрын
ZA MUMBA ZATHEKA CHIFUKWA OKUMBA DZENJE AMAHWELAMO EKHA
@rodglae6657
@rodglae6657 Ай бұрын
Ndiye wagwamoditu Mumba mdzenje lake lomwe.
@JoyceLiwonde
@JoyceLiwonde Ай бұрын
😂😂😂😂Muphana
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn Ай бұрын
Koma ndie zatenga nthawi kuulusako,kukhalangati zisankho zapatatu bwanji
@MosesTangwe
@MosesTangwe Ай бұрын
Mbava zina mpaka kutchula dzina la yehova 🤔
@user-pn6ic9yr1t
@user-pn6ic9yr1t Ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@user-rz8qp8tj8e
@user-rz8qp8tj8e Ай бұрын
Aaaa achithyola which God are you mention now 😂😂😂zithu zikavuta Umalakalaka kuchula Mulungu from morning a till evening 😂😂😂😂ur talking very calmly ngati kamuthu kaulemu 😅😅😅😅
DSS Arrests, Detains NLC President Joe Ajaero +More | Lunchtime Politics
25:48
АЗАРТНИК 4 |СЕЗОН 1 Серия
40:47
Inter Production
Рет қаралды 1,3 МЛН
Men Vs Women Survive The Wilderness For $500,000
31:48
MrBeast
Рет қаралды 67 МЛН
KUYANKHULA MWA MPHAMVU 10 September 2024
26:48
HOT 265
Рет қаралды 917
Zuma's disciplinary hearing to be heard today
5:21
Newzroom Afrika
Рет қаралды 7 М.
NKHANI ZA AFORD NDI PDP PA ZODIAK
16:07
HOT 265
Рет қаралды 8 М.
MOSES KUNKUYU MUTU SUKUKOKA UKU KWANUNKHA UTSI
40:43
Mpungwe-Pungwe mw
Рет қаралды 48 М.
POLICE OFFICERS AND A CIVILIAN IN COURT FOR EXTORTION
Newslive SA
Рет қаралды 338
KUSEMPHANITSA KWA ZIZIMBA, ZOMWE ZINAPHETSA SAULOS CHILIMA 🤯😭
35:46
АЗАРТНИК 4 |СЕЗОН 1 Серия
40:47
Inter Production
Рет қаралды 1,3 МЛН