Basi nankhumwa watha palibe achita nsanje Basi mboleche sangawine malo moti akanagwirizane niazake
@JafferTiles-hp4mu18 күн бұрын
Kutha kwa a Nankhumwa😂😂😂😂
@user-yf5vq3dl5u17 күн бұрын
Kungokula muthu opanda zeru mbuzi ya muthu
@mussamapira80118 күн бұрын
Chakuba ichi chinakumwa amakhala ngati wa DPP koma ali wa mcp ali ngati chiompha nkhanga chomwecho chimangonyosola nyama kumangotaya osanya kungophera njilu wachabe 😢😢😢😢
@user-is5dl7np9g18 күн бұрын
Nankhumwa sangatsogolere dziko la Malawi akudzinyenga chabe
@user-jn2oc3cn3q18 күн бұрын
Kungofuna kuononga nthawi awa Sangakhare president wa Dziko wachulutsa bodza ndikudzikonda yekha
@user-uc1pd1tc2x18 күн бұрын
DPP bomaaaaaa iloooooooo❤❤❤❤❤
@ahmedmsume148917 күн бұрын
Logo ngati security company 😂😂😂😂😂
@user-pl2lj6mh1z18 күн бұрын
Ine gulu uyu amandibowa bwanji
@AbuOsman-ts6ef18 күн бұрын
Mukumana ndi Chala inu
@user-pl2lj6mh1z18 күн бұрын
Anakhumwa galu kwabas
@user-xu2ui5em3i14 күн бұрын
Amp my vote
@user-oj2jr6kf9c18 күн бұрын
Iwe ife ndiye tinapita kale kwa Peter ukunama
@user-lz5tl7gn4v14 күн бұрын
Aaaa zopusa eti ngati ulendo simukatsegula Manda ku mudzi ndi mwayi
@hanifahmponda871118 күн бұрын
Aaaa mutayeni uyoo
@ManzuzoMbawa17 күн бұрын
Dpp❤❤
@Johnybegood26018 күн бұрын
wachamba uyu anguvotere ndani?
@user-gj4li2gc8o16 күн бұрын
Nankhumwa my vote
@user-rc3ze2oi7u18 күн бұрын
Kkkkkkk nakhumwa kumvesa chisaoni
@user-qb1ef1xw5d18 күн бұрын
Wachita bwino kuyambitsa chipani chake nankhumwa limenelo ndiye tsogolo
@user-vl5on2lj8b18 күн бұрын
Kuyambisa chipani chako wachita bwino koma zomwe mwaonesa akulu kosusa tilibe chikhulupiliro painu munkangopanga zamimba yanu osati zaanthu ife president wathu ndi bon kalindo waanthu amphawi.
@MosesNyasulu-lq9sf18 күн бұрын
Eggle chimbalame yowopya anthu tose tizadibwa
@FosterChilumba16 күн бұрын
Angozitu mcp undercover zimatheka bwanji anthu anzeru zawo kugulitsa ufulu wao chifukwa cha ndalama a Yudasi we see u throw
@gabrielben-vj2eb18 күн бұрын
hahahahahahaha...koma dzikoli.....kaaya!
@ElliotOrban-th3qn18 күн бұрын
Koma kummwera anthu akuvutikaa kukakomzesa ma ID and akubwezedwaa so malamulo alibe ntcito
Munthu walephela kusutsa monga iye wa opposition leader mcp kudusa moyela sangakwanise kulamula boma
@user-uf4db7im7d18 күн бұрын
Or atakhala ndi chizindikiro chofanana ngati dpd sangasokoneze a Malawi, anthu adzaona pomwe pali chimanga osati mbalame wagwa naye ameneyo! APM motoooooo Navicha more fire in Parliament
@BenBotolo16 күн бұрын
Forming personal parties is not a solution to our development please avoid forming family parties
@samsonmtumbati485518 күн бұрын
Hot 265 we love you
@hot265.18 күн бұрын
Zikomo Kwambiri bwana🙏🙏
@user-yf5vq3dl5u17 күн бұрын
Wayambisa chipani koma palibe chomwe akuziwa mbuzi ya muthu imeneyi
@zondanitzulumusicfly.520217 күн бұрын
Chiomba nkhanga too much eating beware Malawi kkkj
@ThoccoBondo-mx7vt18 күн бұрын
Nankhumwa manyaka😅😅😅😅
@alexsumani682317 күн бұрын
Pano timveno akhothi ati chani uyu ndiye wayamba chipani chake ,tikungokuonanitu
@JafaliAkimu-ll1bf17 күн бұрын
zitsiru za anthu nakhumwa nkhope mutu ngati phwala
@user-gs7wc3nx3q16 күн бұрын
Kaya zanu izo zivotani muzivutika Nokha ine kuno ku joni niripheee nikudya chicken deyire
@Emmanuelngona875118 күн бұрын
Chilima president and nankhumwa vice president.
@wangachindeya857718 күн бұрын
😅 President wanji opanda ma looks
@mathewssiliya57415 күн бұрын
tikakumana kuseu komweo
@KELVINIDENESS17 күн бұрын
mmm koma agalu awa amatiyesa agalu
@LandiranJubeck17 күн бұрын
PDP security forces
@EstherPeter-cf1vf17 күн бұрын
Zogwilizanatu izi ndi a mcp akufuna aisokoneze dpp akufuna anthu adzabalalike povota cholinga asadzaipeze 50 1 pasana pawo sizintheka zimenezo
@user-xm3zl5cg6x17 күн бұрын
Izi ndi zipan zakuba sorry Malawi samalan ndithu
@user-qj3db4lu7c18 күн бұрын
Kusowa zochita osamakangotsegula Ku Manda bwanji
@JafaliAkimu-ll1bf17 күн бұрын
a mec inu ndiinunso zitsiru
@user-pt8wb4vw6r18 күн бұрын
Nankhumwa yomweyo kuli wawawa zili bwino zipani zose anachita kuyambisa adpp analibe ndi mp yemwe inu pitilini ndi ufulu wanu
@user-jl6sq3ph1b18 күн бұрын
Anakhumwawotu Kaya awonesa zichani zake zimenezo iyeo sangakhaleso president ngakhale patavuta motani ndi mp akuluzaso ameneo 😂
@user-hu6fd8yi7x16 күн бұрын
Sangawine😅
@rashidadan253318 күн бұрын
He is not 2 late , but he is weak , even he was a leader of opposition he done nothing Zipani zonse ndizadyela , inshort
@EmercianahKasiku-en6hl18 күн бұрын
More fire Dr Namnkhumwa dziko likufuna atsogoleri achinyamata opanda matha kunena za kumtima kwawo this is our next president mufune musafune Dr chilima Dr Namnkhumwa Enock chihana,Atupele muluzi dziko lokomera tonse more 🔥
@ManzuzoMbawa17 күн бұрын
Hot 265 umakwana
@user-pj7hn2ky5j18 күн бұрын
😂😂😂 50+1 ukuwona ngt masewera kkkk😅
@FatimaKazembe-ot1os17 күн бұрын
DPP Boma 2025😂😂😂 nakhumwa ndi gawo
@user-be3is8rc4r18 күн бұрын
Zopanda mchere nakhumwa angakhale president 😂
@gabrielben-vj2eb18 күн бұрын
Eti-eti-eti???
@CyprianoSandalamu18 күн бұрын
Nakhumwa yemweyo 2025 more fire
@EmercianahKasiku-en6hl18 күн бұрын
Zamchere nde zija akumakodzedwa asakudziwa adad ali pa msonkhano zija 85 yrs old Gogo kumamulimbikira kit alamulebe Anthu aulesi inu imilani inuyo lija Gogo lakula mwauponda mumafuna muzizasolora muti adadiwo akugona nfi ukalamba 😅😅😅😅 Eagle waona kale sigwira dpp kutha ngati makatani 😢
@mkhulukinyata519815 күн бұрын
Mbuzi ya mano pansi Nan'khumwa..Zaka 4 ukungololera kuti boma lizizunza a Malawi bola iwe ukumatsidwa zammanja , Ndiyeno do you think kuti ndindani yemwe angakhulupilire iwe.. Musapusitse an'thu apa , Amalawi akutulukirani mapulani anu wonse ,Iwe Galu Nankhumwa pamodzi Gwape Frank Tumpale Mwenefumbo", Nonsenu ndinu a MCP up to now, Achayini akenu mukuti kuchalira kuyisokonedza Dpp mu 2025 election .. Mmm mwawuponda .Amalawi 2025 akukasamutsa Mbava zonse zomwe zili ku State House , Ndipo tikukayikako APM ..Even muzabele nkulengezanso kuti Chakwera wawina" Koma Amalawi sadzalora inu kuti muwazunzenso ×2 .Apono ndiye tidzagendanano zogendana basi
@alexsumani682317 күн бұрын
Watha uyu basi
@thulanimpphiri687318 күн бұрын
Nankhumwa chifukwa amayenda ndi mcp zeru walibe chifukwa dpd ndi dpp mukuona pali kusiyana then blue kala chimozimozi ndi dpp.chipanicho abwereso kukapanga bwino bwanji nankhumwa akulimbana ndi dpp
@lazaruschitsamba839418 күн бұрын
koma Malawi muntu wa 80 years akapanga chiyani
@duncainjimmy18 күн бұрын
Ndie omwe sanafike Kuma 80 wa akuchita chani after kulumikizana zipani 9 komabe zakanika kufikira zomwe wa 80 yo anazifikira 😂. Mulungu akutiphunzitsa kulemekeza achikulire ,adadziwa kuti wachikulire amakhala ndimaganizo okhwima ndichifukwanso afikira zaka 80