NKHANI ZALERO-KUYANKHULA KWA ADADI

  Рет қаралды 27,393

HOT 265

HOT 265

27 күн бұрын

Пікірлер: 89
@DawoodIssah-mp1yi
@DawoodIssah-mp1yi 25 күн бұрын
Chitsiru choipitsitsa mdziko la Malawi ndi chimenechi chichakwera, Puppet uyu wa America
@chrisboyce2
@chrisboyce2 25 күн бұрын
Chakwera ndiwopusa Kwambiri bwanji amaleka kuyankhula English kuti America imve koma nkhani ndiyakt ADAD 2025 BOMA!!!💙💙
@user-qt8qe8iu1b
@user-qt8qe8iu1b 24 күн бұрын
Komadi
@Blessingschikadewa-pt6cp
@Blessingschikadewa-pt6cp 23 күн бұрын
Too yomweyo
@simonpaul6567
@simonpaul6567 25 күн бұрын
Bon kalindo he must ne the president of malawi hes the true man.
@MphatsoGona-px6bq
@MphatsoGona-px6bq 22 күн бұрын
Chakwera nd wamakani ekha anati Ngati sipatha zaka ziwiri azatula udindo
@user-xv9en6se4i
@user-xv9en6se4i 19 күн бұрын
APM my vote❤
@user-oq5rg5mz7q
@user-oq5rg5mz7q 25 күн бұрын
Chakwela ndi mbuzi yamunthu,
@user-xi7bo8jx8h
@user-xi7bo8jx8h 22 күн бұрын
Apm my vote
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
@salimmkumakumakitombi-yc7pw 25 күн бұрын
Nde America limazapempha thandizo ngati kumalawi .. .inuyo ndamene muli ndivuto kupempha pempha
@user-jb5yb9wq3y
@user-jb5yb9wq3y 24 күн бұрын
Chakwera walozedwa tikuonera 2025
@NedsonKanjira-qj2ig
@NedsonKanjira-qj2ig 25 күн бұрын
Achita bwino kwambiri Komanso akanabwera akumangeni akulandeninso katundu mukutitenga Ngati zitsiru
@user-jk8sh7fh2d
@user-jk8sh7fh2d 24 күн бұрын
Akuyankhula ngati ali ndipogwilatu koma koma apure ai zikomo bola munakangokhala chete osayankhulapo moti iwe chakwela sukuona kuti kuyankhula uku ndikuzibeleka mbava ku mbuyo , kdi titamati iwe ndie mbava yaikulu nkulakwa? And ndikakhala ine ndinakuziwa kale ndie president oipa ndie sindikuona chodabwisa
@user-qm1qb2jp4s
@user-qm1qb2jp4s 24 күн бұрын
Ife timadziwa timadziwa kuti chakwera ndi chilima tonse alliance nja bodza mmaonjeza ma promise ma guy APM alowe tione Zina ma khoti akumalawi mu nthawi ya tonse alliance sakugwila nthito yokomera malawi chofunika let's work up malawi tikavote tichotse mbavazi
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 24 күн бұрын
APM my vote❤❤❤❤❤
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
@salimmkumakumakitombi-yc7pw 25 күн бұрын
Nanuso kharani pasi .. ACB munaimedza ndangati omwe anamangidwa m,boma lanu ..anthu 83 aja chilima yekha nde anakuphwkerani
@AhmadumkomaTambala-lr9gp
@AhmadumkomaTambala-lr9gp 23 күн бұрын
Thindwa nthawi zonse amasokoneza zinthu
@ShadreckNgozo-ng6ll
@ShadreckNgozo-ng6ll 24 күн бұрын
Kodi nkhani imeneyi mudzakamba liti? Idzaweluzidwa liti? Inuyo manyazi mulibe? Nkhani zakatangale zimatha kuno kumalawi? Sheme on you
@patrickkapinga7091
@patrickkapinga7091 23 күн бұрын
Koma chakwera chomwe akuchifuna achipedza ndithu
@macleanmachamo
@macleanmachamo 25 күн бұрын
America yachita bwino bwanji makhoti akuchedwesa milanduyo
@user-ev6bi7jr7g
@user-ev6bi7jr7g 23 күн бұрын
Chilichonse chabwino chomwe angapange a MCP panopa chifukwa ndi kampeni ili ndi cholinga chofuna kukopa anthu
@SinyoroMoyo
@SinyoroMoyo 22 күн бұрын
Chakwera m'busa odya chakhumi
@ophlexmkondowe8107
@ophlexmkondowe8107 24 күн бұрын
Koma ku bomako kuba kwanyanya mpaka America kulankhulapo,mmati DPP ndiyakuba nanga mwamanga angati,ndale zopusa.
@user-ik8ii8nv1i
@user-ik8ii8nv1i 23 күн бұрын
America yachita bwino powatsekera akubawo
@AubreyChiyaya-ty8ge
@AubreyChiyaya-ty8ge 24 күн бұрын
Mwana wa hule chakwela
@user-xm3zl5cg6x
@user-xm3zl5cg6x 24 күн бұрын
American imata kwambili ntati zakuwawa chakwela uwamenye tikuwonele mbava iwe ukuwopa Tanzania kuli bwanji America opusa iwe ndithu
@HanishaissahKagansa
@HanishaissahKagansa 25 күн бұрын
Mawu awawa akupita kwa American komano American imva nao chichewacho 😂😂😂😂😂😂
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 24 күн бұрын
Kufoira kmso mantha .😂😂
@elishamael-shadai
@elishamael-shadai 25 күн бұрын
Where are the 83 criminals you promised to get arrested including you Chakwera
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 24 күн бұрын
America yangon'alura chilungamo bravo achitsiru apule mudya chani mukanyoza America shut up
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem 24 күн бұрын
President opusa kwambili nde uzikapepha kut galu iwe popeza ndi Baden yemweyo umakamugwadira
@user-qp4gk5gx8j
@user-qp4gk5gx8j 23 күн бұрын
Yes but ndizzoonaaa
@user-td1ll5ge6n
@user-td1ll5ge6n 24 күн бұрын
Mbuzi imene bola awamasula khontiso lachani😊😊😊😊
@geraldtuwaga-iz6ll
@geraldtuwaga-iz6ll 24 күн бұрын
Kodi chakwera yu akufuna kunama Kuti ACB ikugwira ntchito Malawi Muno?
@user-cy7gd1go6y
@user-cy7gd1go6y 23 күн бұрын
Chakwera ndi mbuz
@user-vu9rt8gj3o
@user-vu9rt8gj3o 25 күн бұрын
Chakwela ndiwee galu wamuthu
@user-xt2gu9yt9q
@user-xt2gu9yt9q 25 күн бұрын
Kulakhula kwa apule chimozimozi Mwana weniweni ndalama dzakunja kwake kuti simwati ndiauba paka apule kunena ameleka kuti ndiokuba koma soka lapamalawi ukalodzedwa sunukha
@homeremedys3748
@homeremedys3748 23 күн бұрын
Ngati bodza kuti wamwalira Nkaka, sleep well Nkaka
@WisikiBlack-gj4gu
@WisikiBlack-gj4gu 25 күн бұрын
Iwe supanga nawo ndiweso mbamva, paka America yakuonelani achakwela
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 25 күн бұрын
Ndipo why am alankhula chichewa podzudzula America yo, uyu ndi krook kwambiri mweeee... Inu nonse ndi mbava di zooona zokhazokha..
@user-xt2gu9yt9q
@user-xt2gu9yt9q 25 күн бұрын
Analowa 2020 boma thawiyosei bwanji samachitapo Kathu padzandalama dzamisokho yaabusawa apanga pano kamba ka kapeni tiyeni mutipedza usogoloko
@user-zg9se4rw6v
@user-zg9se4rw6v 24 күн бұрын
Osatukwana, bwanji kodi
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 24 күн бұрын
Chakwera ndi mfiti guys, nyumba ya zipinda zitatu anthu tiziimanga dzaka 23 mmmmm coz chakudura kwakatundu mmmmm😢😢😢😢😢😢😢
@ThokohKalonga-je9rx
@ThokohKalonga-je9rx 24 күн бұрын
Ndingaipedze bwanji Vedio imeneyi Kuti ikhale muphone mu
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 24 күн бұрын
America or kukhale zochitika zambiri koma zawo zikuyenda and America palibe chimene ingatenge kuno ku African chauleri imagula. Koma inu apule ndi benja lanu mumapita ku America kukapempha.so dolo ndindani mukukhzikisa zikopa alendo alendo mukufuna azibwera kumalawi wochokera ku America nanga America yingakope alendo kuchoka kumalawi ndakauika
@isaaczidana2914
@isaaczidana2914 24 күн бұрын
Boma ili ndilakuba America yachitabwino .
@beinhardkausiwa7107
@beinhardkausiwa7107 25 күн бұрын
Achakwera nthawi yanu ndiye ikufulumira kuthatu....APM akulowa next year ku sanjika palace....chifukwa chani ukuikira kumbuyo mbava?kodi kapena mumabera limodziiii?
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 24 күн бұрын
APM woyeeeeeee ❤❤❤❤
@alexmkolongo3089
@alexmkolongo3089 24 күн бұрын
Akuyikila kumbuyo anthu akuba uyu
@adamkudzala186
@adamkudzala186 24 күн бұрын
Anangolakwa nayenso osamupanga bar chifukwa nayenso ndiwakuba
@WilsonLimited-os1xd
@WilsonLimited-os1xd 25 күн бұрын
2025 bon kalindo Bomaaa ati ngati niseke kkkkkk
@user-qm1qb2jp4s
@user-qm1qb2jp4s 24 күн бұрын
Nsonkho kungochotsera abusa okha bwanji komanso mu nthawi ya kampeni kwanji???
@LingtonChimutu
@LingtonChimutu 24 күн бұрын
Bomatu iro kazaramurani i
@user-qp5mu7ui2c
@user-qp5mu7ui2c 25 күн бұрын
Uyu akusiwa chilungamo
@JohnConar-kq4hi
@JohnConar-kq4hi 23 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 achakwera njenje aseka ma account awo
@user-ln3zx6wo4w
@user-ln3zx6wo4w 24 күн бұрын
Mbava zimabakiranatu
@LuteSynos
@LuteSynos 24 күн бұрын
Amangidwe mayiyo
@user-xj9uy6wz7b
@user-xj9uy6wz7b 24 күн бұрын
Esh
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du 24 күн бұрын
Chakwera ndi galu iweso
@tisuhmakhwah7085
@tisuhmakhwah7085 24 күн бұрын
Just translate it into English amarica yo imve bwnobwino .. president opepela uyu watikwana😅😅😅
@user-nu8oo6oc4j
@user-nu8oo6oc4j 24 күн бұрын
Mesa iweyo galu papet WA biden
@promixphotography8056
@promixphotography8056 24 күн бұрын
Baga moyo wachakwera
@user-fp5qn5ci2v
@user-fp5qn5ci2v 25 күн бұрын
Mmm makhoti akuno amatha ntchito ntchito yake iti ziphuphu zomwezo?
@mayesojameskatete
@mayesojameskatete 25 күн бұрын
Lazaro waumphawi basi bagamoyo 😂😂😂
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 24 күн бұрын
😂😂😂😂😂
@chrismatemba556
@chrismatemba556 25 күн бұрын
Wasting your time. This country is going no whete with bad reputation of our own making. Do not blame anyone but ourselves. Especially, politicians.
@mussazilingo4544
@mussazilingo4544 24 күн бұрын
Pamenepo akuganiziratu DPP 😅
@macleanmachamo
@macleanmachamo 25 күн бұрын
Apule mwapupuluma poyankhapo
@MphatsoGona-px6bq
@MphatsoGona-px6bq 22 күн бұрын
Timakukondani adad Dpp boma 2025.....
@malawigeneralguide1646
@malawigeneralguide1646 24 күн бұрын
Zakupoila Kwa a pule aliyense akuziwa kale Koma prophet yo amangidwe tisanamugende😡😡
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l 4 күн бұрын
Galu mbava yayikulu mumalawi, racist president chiyenda chekha chopanda mwana
@duncainjimmy
@duncainjimmy 24 күн бұрын
Ngati America amapempha ku Malawi ndie kuti Chakwera is right koma ngati America without Malawi singavutike then Chakwera is wrong
@thondoyaenterprise3795
@thondoyaenterprise3795 25 күн бұрын
America has just banned those 4 from entering their nation. I dont see any meddling their.
@user-fm8ed7eo3i
@user-fm8ed7eo3i 25 күн бұрын
American yachita bwino kuwaletsa koma a chakwera chifukwa cha Kuba kwambiri ndi momwe akuyikira kumbuyo anthuwo
@simonpaul6567
@simonpaul6567 25 күн бұрын
All those you what you talking it can not work dtop down building materials then people then pwople the can manage to build nice houses
@simonpaul6567
@simonpaul6567 25 күн бұрын
This government is stupid indeed
@user-oe1lg4xo7w
@user-oe1lg4xo7w 24 күн бұрын
Chakwara ndi nzibanbo ombwambwana koma nkaziwake samazuzula mamunayi?
@hazibatizoni9366
@hazibatizoni9366 24 күн бұрын
Why speech imeneyi osayankhura muchizungu kut dziko la America live😂
@JonesChingaya-yf4gg
@JonesChingaya-yf4gg 24 күн бұрын
Ngat pali nthawi imene mdzika za dziko lino zinataya ma voti awo pa chabe, pamaloto a chumba ndie 2020 povotera Tonse alliance ndi Chakwera, stupid President ever. Mfumu yeniyeni ya katangale.
@NuradinaAbrahima-rt9ip
@NuradinaAbrahima-rt9ip 24 күн бұрын
Chakwela ndiwe munthu woyipa kwambili stupid ☹☹☹☹
@simonpaul6567
@simonpaul6567 25 күн бұрын
Malawian court of the law donsnt work well at all to people of malawi ,because court of malawi they under mcp.
@DawoodIssah-mp1yi
@DawoodIssah-mp1yi 25 күн бұрын
Uku ndi kupusitsa Amalawi iwe chakwera ndi mbuye wakoyo America Get out all of you puppets
@WilsonLimited-os1xd
@WilsonLimited-os1xd 25 күн бұрын
Ghetto master munthalika katundu
@user-vu9rt8gj3o
@user-vu9rt8gj3o 25 күн бұрын
Chakwela ndiwee galu wamuthu
Glow Stick Secret (part 2) 😱 #shorts
00:33
Mr DegrEE
Рет қаралды 30 МЛН
Зу-зу Күлпәш. Стоп. (1-бөлім)
52:33
ASTANATV Movie
Рет қаралды 795 М.
【獨生子的日常】让小奶猫也体验一把鬼打墙#小奶喵 #铲屎官的乐趣
00:12
“獨生子的日常”YouTube官方頻道
Рет қаралды 106 МЛН
Don’t take steroids ! 🙏🙏
00:16
Tibo InShape
Рет қаралды 25 МЛН
The Times Malawi Report: CCPF Impresses South African Officials
2:51
Skeffa Chimoto Apresident new Audio Official
8:35
Yathu Music Official
Рет қаралды 72 М.
HOT CURRENT 🔥 🔥 🔥 12 May 2024
25:53
HOT 265
Рет қаралды 12 М.
Misomali Ya Six Inches Yothana Ndi Zipani Zotsutsa - Bon Kalindo
17:18
ZOCHITIKA ZA BRIAN BANDA 🙌🙌🙌🙌
22:25
HOT 265
Рет қаралды 16 М.
Glow Stick Secret (part 2) 😱 #shorts
00:33
Mr DegrEE
Рет қаралды 30 МЛН