America ayenela kulankhula chifukwa ndi ayini ake a ndalama ,it's painful kumaona kuti akutumiza Thandie wina mkumaika mthumba make Malo mothandizila anthu Osauka
@chitanibenito110923 күн бұрын
Kumangoti ma court, ma court ake ati??? America sinalakwise coz too much delays ma court anthu especially milandu yeni yeni osati za born kalindo anthuwa onse ngakuba chakweraso ndiye mbudzi yeni yeni.
@rashidadan253323 күн бұрын
MALAWl has destroyed because of Chakwela and his cabinet and his family , I will Happy to see this Crue are arrested , big criminals in MALAWl , We don't have court of justice here in MALAWl because all of them are under corruption of this particular government of MCP
@WisikiBlack-gj4gu23 күн бұрын
Chilungamo chili poyela apa abale palibe zozungulila zungulila apa ,milandu paka ifike 2025 kuma vote 🗳 chigamulo chizakhala liri?
@patassonelucaszovuta343123 күн бұрын
Kodi olo inuyo a kunkuyu mungalole kuti munthu amene ali ndi mbili yakuba adzibwela kunyumba kwanu kumadzacheza ndizachidziwikile kuti munthu wakuba sitimulola kubwela kunyumba kwathu
Zoti a Malawi adziwe nzoti milandu ku Malawi kuno ndi a ife osauka chifukwa siyimatenga nthawi kutha Ku ma court koma zandare pa nkhaniyi ayi. President wanthu afulumira ovutika tinkhara ifeyo common people. Chonde iwo a pepese
@WisikiBlack-gj4gu23 күн бұрын
Yes zoona zikanateladi kumbali,,koma chakwela inamukhudza khani ija, chifukwa mu athu akatangalewo chakwela alimo,chifukwa walupha malile kuesa kuzibisa koma ziululika zayamba kale man chakwela
@user-pv9uk6sc3w23 күн бұрын
President chakwera sadaganize polankhula kunyoza America, akukhala ngati akugwirizana ndi kuba.
@JIMMYWATHONJE23 күн бұрын
Chakwela the fool of the foolest
@WisikiBlack-gj4gu23 күн бұрын
Ma jaji athu palibe ilipo alimumbuyo ma boma lachakwela akupanga business ndichakwela ,,mukhani zakatangale
President akuziwapo kanthu, ndithu. And kufufuza mpaka ati 4 years akufufuzabe , aaaaaah koma amene anatilozayo ndi emweyo tili ndi vuto la muwubongo makamaka akuluakulu ku ntundaku zosaenda . Ma mericans-wa ndie kuti anafufuza kale pa okha why inu mukuchedwa pa zifukwa zoti nonse ndi akuba ndie ndi zovuta kuti akuba okhaokha sangayalusane. Ndie angoona kuti anthuwa ndi amozi asatipusise tingowauza zochita bsi eyetu.
@JafaliAkimu-ll1bf23 күн бұрын
chakwera ndi chitsiru zamukwana ban imeneyi chifukwa iye ndimbavanso yayikulunso
Chakwera ndi chitsilu amaleka kuyakhula chizungu chakwa America bwanji
@user-og8qm5qx8f23 күн бұрын
Zozungulira ayi tangoyankhani mafunso komanso palibepo mbalume pamenepo ndi Street thing answer the question pls
@paulmakaula493722 күн бұрын
America has followed its laws as quoted, the bsn is applied in America not Malawi...in Malawi they're free and relaxed BUT not America, they don't entertain those issues
@petertaulo801423 күн бұрын
America yachita bwano kutelo
@ShabaniKuswere22 күн бұрын
Ndeakuti ma Court anthu akumalawi amatha kugwira ntchito kuposa America????😂😂😂 Koma Chakwera guys i think wapenga
@kubengovender699623 күн бұрын
Alibe mphatso yawu president!!
@petertaulo801423 күн бұрын
Kumkuyu garu wa munthu.
@user-og4oe5yp4w22 күн бұрын
Dziko la malawi limadalu
@johnjoachim382023 күн бұрын
Support criminal adha awa and wina akamati amuvotela😮
Makhothi ake ati,???? Ku Malawi kulibe mathoti anapangidwa Captured ndi mcp ngati injunction ya nankhumwa kutha years nde milandu zinazi anga kambe.. Tinawombera mfiti mmanja...
@jonathanmalanda774223 күн бұрын
Amalawi ku opa America dziko lopanda yankho pa lokha
@bensonmughandira23 күн бұрын
😂Galu wankota sakandira pachabe.les wait and see. wait
@user-yk3wc9ei5g22 күн бұрын
Chakwera is corrupt,thats why he is defending those people.
Ukamamubwezera mawu munthu okuzuzula zimangowoneseratu kuti ukuvomereza kulakwakwako . Kunena zowona boma lachakwera ndirazimbava ndipo makhoti onse Akulamuliridwa ndi chakwera ndi chipanichake cha mcp. Akunkuyunso sangalankhule chirungamo chifukwanayenso ndibamva.
@ShabaniKuswere22 күн бұрын
Kodi kumkuyu mmutu mwake mulimzeru?
@alexmkolongo308923 күн бұрын
Sizikugwilizana watsala iwe
@chipanganofackison518522 күн бұрын
Guys ma American siwofunika kumawasekelera eya zowona amapereka mathandizo Koma amakhara ndicholinga mudzikomo pamapeto adzakupusitseni then atenge zofunazo mosavuta and we need to know dziko lirilose limene mulimikangano ma American akango yamba kulowelerapo mapeto ake dziko limalowa nkhondo mcholinga azidzapangamo ma businesses azida zankhondo president wa Malawi akadapanda kulankhulapo mukadatiso ndiwogona kwambiri
@user-hx6ly3cl8m23 күн бұрын
Makhot anthu akugwila ntchito ndi emusip
@JafaliAkimu-ll1bf23 күн бұрын
kumkuyunso ali limodzi muwumbsva
@user-og4oe5yp4w22 күн бұрын
Dziko la Malawi limadalira kuphepmpha ku america komweko ndiye americawo awone zochita basi
@user-zl8fl7yp8q21 күн бұрын
Musavutike ndi kuganizaso chakwera ndi mbava.akanakhara wanzeru akanat America yandithandiza athuwa ndimbavadi
@user-uv7yq1fx4r23 күн бұрын
Makondela inu koma akanakhala azipani zina bwezi mutamanga kalekale
@YohanePatrick-lc2lq23 күн бұрын
American tsinalakwe chakwelalayo ndiye wakuba kwambili mbava dzokhadzokha sitikumu funa pamozi ndi kunkuyu achoke dpp boma 2025 tatopa komaso joice banda usiletu kunamidza athu komaso athu muchenjele Joyce anaba ndalama ya ndege anayda yekha ndiye chenjelani mudza wona mavuto ngati womwewa komasotu Joyce banda alinali ku mcp motelo idzi akupanga dala akupanga akufuna kuti dpp isawine ku mwela akufuna dpp ndi pp pakati akudziwakale kuti mcp ndiyo winawina kale chonde amalawi musapange mistake kawili Joyce ndiwo tsokonedza my name is Patrick form South Africa
@violetnkhoma853523 күн бұрын
Koma abaalee 😂
@user-zg9se4rw6v23 күн бұрын
Eee achita bwino pule akwiya
@CyprianoSandalamu23 күн бұрын
America sadalakwitse ,manyumba mwathu,tikaona kuti mwana wathu akuba,amasalidwa ndi abale amakolo Ake kuti asabwere kunyumba kwathu, chifukwa Cha mbiri yakuba,ndiye dziko Lili ndi anthu akuba ndye ma mericans asekere zupusazo?
@JonesChingaya-yf4gg22 күн бұрын
You are not honest Mr President, kutha mau chifukwa aletsa mbava kulowa dziko lawo?? Mr President mukanakhala wina mukanauza a ma court athu azifulumiza milandu osat mpaka 4yrs milandu isanathe. Munthu womvesa chisoni Chakwera.